Kulimbikitsa kukhala ndi nyelele mmunda wanu wa zipatso

Nyelele zofiira ndi bwenzi la alimi. Zimateteza zipatso ku atongole ndi tizilombo tina.Ngati mulibe nyelele zofiila zimenezi mmunda wanu, tolerani zitsa ndi kukadziyika mu umodzi mwa mitengo ya zipatso zanu.Thandizani nyelele kupita mitengo yina pomanga chingwe kapena kuyala kamtengo kulumikiza mitengo yoyandikana

Current language
Chichewa / Nyanja
Need a language?
If you would like this video translated into other languages, please contact kevin@accessagriculture.org
Translated in
Malawi
Translation funded by
GIZ
Uploaded
3 years ago
Duration
13:00
Produced by
Agro-Insight