Kulima ndiwo zamasamba mu madimba oyandama pa madzi
Pomwe minda yathu yikukhala mmadzi osefukira nyengo ya mvula, makolo athu ankaganiza njira zolimira mbewu kuti tikhalebe ndi chakudya. Anapanga madimba oyandama pamadzi pogwiritsa ntchito zinyalala zotsalira ku mbewu. Sitimafunanso fetereza kapena mankhwala ophera tizirombo, chifukwa bedi loyandama limakhala ndimanyowa achilengedwe.
Current language
Chichewa / Nyanja
Available languages
Need a language?
If you would like this video translated into other languages, please contact kevin@accessagriculture.org
Translated in
MALAWI
Translation funded by
GIZ - KCOA
Uploaded
1 year ago
Duration
14:15
Produced by
CCDB